Kuno ku Naizi tikupempha nawo Bin ya zinyalala pa Msika
Kuno ku Namiyango area ya cha pa Tondole magesi akumavuta kwambiri
I would like to commend Blantyre City Council and the organisations they are in partnership with for the construction and rehabilitation of public toilets.
Ine monga m'modzi mwa anthu okhala kuno ku Zolozolo East ndati ndikambepo mobwereza kuti papita nthawi pamene ntchito yomalizitsa kumanga health centre idayima. Tikufuna Khansala wathu komanso aKhonsolo ya Mzuzu adziwe kuti Health Centre imeneyi itha kutithandiza kwambiri kotero kuchedwa koti iyambe kugwira ntchito tikumva nako kuwawa
Ma paipi amadzi ambili anthu akumaononga mosavuta chifukwa ena ndi aplastic sangapange dongosolo loti onse akhale achitsulo?
Tati tidandaule nkupanga report kuti kuno ku Ndirande vuto lakuzimazima kwa magetsi likupitirira. chonde atithandize.
Kuno ku Area 24 pafupi ndi panyenye stage pipe ya madzi ya water board yaphulika
I would like to express my appreciation to ESCOM that for this whole week we have had power supply continuously here in Area 25.
kuno ku Chilinde tikuthokoza kuti khansala wathu adakamba ndi a-chibuku ndipo pano pamalo pomwe sipadali bwino chifukwa cha kuunjikana kwa zinyalala akonza
Ndati ndidziwitse khansala wathu kuno kwa Tsabango 2 kuti tikudikirabe lonjezo lawo loti adzaitanitsa msonkhano kuti anthu tikakambirane za mavuto omwe alipo kudera lathu,
In Zolozolo West; the road from CCAP through Bagidadi area needs upgrading. We engaged our councilor before and we were told that it is amongst the roads for consideration under the MASAF project but we don’t know when.
1. The city council should step up efforts in waste collection. For some areas they should not stick to their program of collecting waste twice a week. Waste should be collected as and when the waste storage dustbins in designated places are full 2. The city council should not focus on chasing people selling merchandise along the streets but rather find a long lasting solution like expansion of existing markets or erection of new markets in strategic locations. 3. We would be happy if information on expenditure under various projects such as the Local Development Fund is shared with the public; by pasting on boards at the city council and or promoting initiatives by councilors to share with citizens through their respective ward committees. 4. The city council should be strict with regards giving out business operation licenses for drinking joints. In some areas Bottle Stores are very close to people’s houses. 5. Indians should not be allowed to reside in rooms that are a floor above their shops in town. When they hang their clothes and blankets that have been washed the city does not look good. Especially in Limbe.
Michiru area after Sonke's junction behind mbiridzi's residence. Two pipes on same road akutaya madzi mochuluka
1.The Mayor should take an initiative to ensure the city council is strict on infrastructure planning. The city of Mzuzu should not have poorly designed and constructed structures. 2. The Mayor should establish vibrant Mayor’s trophy competitions as our counterparts in Blantyre do. This helps in promoting information sharing amongst the youth and helps in ensuring the youth desist from immoral behaviors. 3. We have heard about reports of abuse of resources at the city council, the Mayor should come out clean on this and ensure concerted efforts with fellow councilors so that this does not continue.
Am glad that one of the candidates for the position of Mayor showed up and he has really good plans for mzuzu even though we dint hear the plans that the others have. The tricky part is that the whole mayorship position will be determined by 15 people with half of them being from the opposition side. Grace Lynn - Mzuzu